Mawu a M'munsi
b Kuti ithandize ana kukhala ndi chikhumbo cha chidziŵitso cha m’Baibulo, Watch Tower Society inatulutsa zithandizo za kuphunzira Baibulo zopepuka, zonga Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo ndi Kumamuvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo. Mabuku onse aŵiriwa amapezekanso pa matepi a mawu.