Mawu a M'munsi
a Catechism of the Catholic Church inayamba kufalitsidwa mu 1992 ndipo inalinganizidwa kuti ikhale maziko a chiphunzitso cha Akatolika padziko lonse. M’mawu ake oyamba Papa John Paul II akuifotokoza kukhala “malembo owagwiritsira ntchito otsimikizirika ndi odalirika ophunzitsira chiphunzitso chachikatolika.” Katekizimu ina ya Chikatolika chapadziko lonse yonga imeneyi inatulutsidwa mu 1566.