Mawu a M'munsi
b Nthendayo ingafalikirenso mwa kuika mwazi ndi kubwerekana majekeseni obayira anamgoneka m’mitsempha. Akristu ena opanda chifukwa atenga nthendayo kwa anzawo a muukwati amene anachita chisembwere kapena kugwiritsira ntchito anamgoneka.