Mawu a M'munsi
a Chenjezo la Paulo pa 1 Akorinto 7:1 la “kusakhudza mkazi” mwachionekere limanena za kugonana, osati kumkhudza wamba. (Yerekezerani ndi Miyambo 6:29.) M’nkhaniyo, Paulo akulimbikitsa umbeta ndi kuletsa kudziloŵetsa m’chisembwere.—Onani “Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga” mu Nsanja ya Olonda ya January 1, 1973 m’Chingelezi.