Mawu a M'munsi
b Ena mankhwala amawayambukira moipa, kuwapatsa nkhaŵa ndi zovuta zina za mtima. Ndiponso, mankhwala othandiza kuwongokera angawonjeze kunyikuka mwa odwala matenda onyikula monga Tourette syndrome. Chifukwa chake dokotala ayenera kuyang’anira kaperekedwe ka mankhwalawo.