Mawu a M'munsi
a Liwu lakuti “Aamazon” likuoneka kuti likuchokera ku liwu lachigiriki lakuti a, lotanthauza “alibe,” ndipo ma·zosʹ, limatanthauza “maŵere.” Malinga ndi nthanthi zakale, Aamazoni anachotsa bere lawo la kulamanja kuti azigwira bwino uta ndi muvi.