Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Zitsogozo za mu 1995 zimagwira ntchito kwa misinkhu yambiri koma osati yonse. “Ambiri akuvomereza kuti zitsogozo zatsopano za kulemera kwa thupi sizikugwira ntchito kwa anthu azaka zoposa 65,” akutero Dr. Robert M. Russell mu JAMA ya June 19, 1996. “Ndipotu kunenepa pang’ono kwa munthu wokalamba kungakhale kopindulitsa popeza kumasunga nyonga yogwiritsira ntchito atadwala ndi kuthandizira minofu ndi mafupa kukhala yolimba.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena