Mawu a M'munsi
a Kaŵirikaŵiri mlingo wa phokoso umadziŵika mwa kugwiritsira ntchito chipangizo chimene chimapima phokoso mwa ma decibel. Pakuti khutu limamva bwino chiunda cha mapokoso ena kuposa cha ena, chipangizocho chinakonzedwa kuti chizilabadira mofananamo.