Mawu a M'munsi
a Nkhani ya Watergate inatchulidwa choncho chifukwa chakuti nkhaniyo inaululidwa ndi anthu ena amene analoŵa mokakamiza m’nyumba yomwe inali kutchulidwa ndi dzinalo. Zimenezi zinachititsa Pulezidenti Richard Nixon wa U.S. kutula pansi udindo wake ndiponso kumangidwa kwa alangizi ake akuluakulu angapo.