Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Madokotala ena amati ngati muona kuti kuchita zimenezi nkovuta, kaziyesezani ngati kuti mukuchita zimene mumaziwopazo. Yerekezerani mukumalingalira zinthuzo mwadongosolo lake bwinobwino. Nkhaŵa yanu ikhoza kuyambika; koma pitirizani kumadzikumbutsa kuti zitheka kuti ena satsutsa zimene mufuna kuchita, kapena ngati angatsutse, sizikhala zoipa kwambiri kusiyana ndi zimene mukuganiza ndipo lingalirani mapeto a zochitikazo ngati kuti zatha mmene mumafunira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena