Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu anayesapo kuchirikiza malamulo oletsa zinthu ameneŵa mwa kupotoza Malemba. Ngakhale kuti Baibulo silimanena zinthu ngati zimenezo, wazaumulungu wina wotchuka wotchedwa Tertullian ankaphunzitsa kuti popeza mkazi ndiye anachititsa “tchimo loyamba, ndi manyazi . . . a kutembereredwa kwa anthu,” akazi ayenera “kuyendayenda monga Hava, akumalira ndi kulapa.” Mpaka analimbikira kunena kuti mkazi wokongola mwachibadwa ayenera kumabisa kukongola kwakeko.—Yerekezerani ndi Aroma 5:12-14; 1 Timoteo 2:13, 14.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena