Mawu a M'munsi
a Yomwe imatchedwa kuti nkhondo yauve inachitika panthaŵi imene bungwe la asilikali linkalamulira (1976—83) pamene anthu ambiri amene ankaŵaganizira kuti ndi oukira anaphedwa. Ena amayerekezera kuti chiŵerengero cha omwe anaphedwa ndi pakati pa 10,000 ndi 15,000.