Mawu a M'munsi
b Mongoyerekezera chabe, ku United States kokha kuli anthu ogontha okwanira miliyoni imodzi, olankhula “chinenero chawochawo ndipo okhala ndi chikhalidwe chawochawo.” Ameneŵa anangobadwa ali ogontha. Ndiponso pali anthu mwina okwanira mamiliyoni 20 omwe samamva kwambiri koma amalankhulana ndi lilime la amayi wawo.—A Journey Into the Deaf-World, buku lolembedwa ndi Harlan Lane, Robert Hoffmeister, ndi Ben Bahan.