Mawu a M'munsi
a Galamukani! sichirikiza machiritso a mtundu ulionse. Akristu ayenera kulingalirapo bwino okha, kusamala kuti machiritso alionse amene asankha sakuombana ndi mapulinsipulo a Baibulo. Ena sayenera kutsutsa kopena kuweruza pa zimenezo.