Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zimenezi sizinachititse kuti akazi asanduke anthu otsikirapo m’mabanja, kuti iwo ndi oyenera ntchito za m’nyumba kapena za kumunda basi. Zimene Baibulo limafotokoza za “mkazi wangwiro” m’buku la Miyambo zimaonetsa kuti mkazi wokwatiwa sankangosamalira banja lokha komanso ankasamalira zinthu zambiri za pakhomo, ankalima n’kumapeza chakudya chokwanira, ndiponso kugulitsa malonda.— Miyambo 31:10, 16, 18, 24.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena