Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti mawu akuti “moyo umene munthu amayembekezereka kukhala” ndi akuti “utali umene anthu ambiri amatha kukhala ndi moyo” nthaŵi zambiri amatchulidwa ngati amodzi, mawu aŵiri ameneŵa ndi osiyana. Mawu akuti “moyo umene munthu amayembekezereka kukhala” amatanthauza kuchuluka kwa zaka zimene munthu angayembekezere kukhala ndi moyo, pamene mawu akuti “utali umene anthu ambiri amatha kukhala ndi moyo” amatanthauza kuchuluka kwa zaka zimene anthu ena ake paokhapaokha amakhaladi ndi moyo. Motero, chiŵerengero chongoyerekezera cha moyo umene munthu amayembekezereka kukhala chimapezedwa poona utali umene anthu ambiri amatha kukhala ndi moyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena