Mawu a M'munsi
c Ngati mukufuna kudziŵa zambiri zokhudza mmene mungakonzere mosavuta malo anu okhala, onani nkhani zakuti “Kukumaniza Chitokoso cha Udongo” ndi ina yakuti “Zimene Zimakupatsani Thanzi—Zimene Mungachite,” mu nkhani za Galamukani! za September 8, 1998 ndi April 8, 1995.