Mawu a M'munsi
a Onani nkhani yakuti “Lingaliro la Baibulo: Kodi Ana Ayenera Kudzisankhira Chipembedzo Chawo?” mu Galamukani! wa March 8, 1997 masamba 26-7. Onaninso, masamba 24-5 a bolosha la Mboni za Yehova ndi Maphunziro, lofalitsidwa ndi Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania, 1995.