Mawu a M'munsi
a Mboni za Yehova zathandiza athu miyandamiyanda kulandira uthenga wa chiyembekezo wa m’Baibulo kudzera m’phunziro la Baibulo lapanyumba laulere. Mungathe kukonza kuti adzakuyendereni polembera kalata kwa ofalitsa magazini ino kapena popita ku Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova ya kumene mumakhala.