Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a “Matenda a shuga akapanda kuchiritsidwa amayambitsa ketosis. Imeneyi imayamba chifukwa cha kuchulukana kwa ma ketones m’thupi, zotsala mafuta atagaika m’magazi; kenako pamatsatira acidosis (kuchulukana kwa asidi m’magazi) komanso kumva mselu ndi kusanza. Pamene thupi ligaya zakudya zopatsa mphamvu ndi mafuta koma kugayako osayenda bwino, zotsala zapoizoni pakugayapo zimachulukirachulukira m’thupi, ndipo wodwalayo amakomoka.”—Encyclopædia Britannica.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena