Mawu a M'munsi
a “Matenda a shuga akapanda kuchiritsidwa amayambitsa ketosis. Imeneyi imayamba chifukwa cha kuchulukana kwa ma ketones m’thupi, zotsala mafuta atagaika m’magazi; kenako pamatsatira acidosis (kuchulukana kwa asidi m’magazi) komanso kumva mselu ndi kusanza. Pamene thupi ligaya zakudya zopatsa mphamvu ndi mafuta koma kugayako osayenda bwino, zotsala zapoizoni pakugayapo zimachulukirachulukira m’thupi, ndipo wodwalayo amakomoka.”—Encyclopædia Britannica.