Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Kufufuza kwaposachedwa kwasonyeza kuti kuphatikiza mkaka wa m’botolo ndi mkaka wa m’maŵere kungakulitse tsoka lakutenga kachilombo ka HIV ndipo kuti mkaka wa m’maŵere ungathe kukhala ndi mankhwala amene angathe kufoketsa kachilomboko. Ngati zimenezi zili zoona ndiye kuti chosankha chabwino chingakhale kuyamwitsa mkaka wa m’maŵere koma mosamala, ngakhale kuti njirayi ili n’zovuta zina. Komabe, pakali pano palibe umboni wonse wotsimikizira kufufuza kumeneku.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena