Mawu a M'munsi
b Onani Galamukani wa May 8, 2000 pa mutu wakuti, “Achinyamata Akufunsa Kuti. . . Kubereka Ana—Kodi N’kumene Kumachitisa Mwamuna Kukhala Weniweni?” Kuti mumve zambiri za mavuto a kukhala mayi wosakwatiwa kwa atsikana, onani Galamukani! wa May 8, 1986 pa mutu wakuti “Achichepere Akufunsa . . . Umayi Wopanda Ukwati—Kodi Zingachitike Kwa Ine?”