Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Chilamulo cha Mose chinalamula kuti mwamuna amene wachimwitsa namwali am’kwatire. (Deuteronomo 22:28, 29) Ngakhale zinali choncho, sikuti zikatero ukwati umangochitika ayi, chifukwa bambo wa mtsikanayo amatha kukaniza. (Eksodo 22:16, 17) Ngakhale kuti Akristu lerolino sali pansi pa Chilamulo, zimenezi zikutitsimikizira za kuopsa kwa tchimo la kugonana ukwati usanachitike.—Onani “Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga” mu Nsanja ya Olonda ya November 15, 1989.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena