Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Galamukani! si magazini ya zamankhwala, ndipo nkhani za matenda a MCS sizinalembedwe n’cholinga chofuna kuchilikiza chithandizo cha mtundu winawake. Nkhanizi zikungofotokoza za njira zimene zatulukiridwa posachedwapa komanso njira zimene madokotala ena komanso anthu odwala matendaŵa aona kuti ndi zothandiza polimbana ndi matendaŵa. Galamukani! ikudziŵa kuti madokotala sagwirizana pankhani ya gwero la MCS, mmene matendaŵa amakhalira, kapena chithandizo ndiponso ndondomeko zambirimbiri zoperekedwa ndiponso zogwiritsidwa ntchito ndi odwala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena