Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Chitsanzo chodziŵika bwino kwambiri cha vuto la ma enzyme ndi cha enzyme yotchedwa lactase. Anthu amene ali ndi vuto la lactase, matupi awo satha kugaya lactose wa mu mkaka, ndipo amadwala akamwa mkaka. Anthu ena alibe enzyme yokwanira yogaya tyramine, mankhwala amene amapezeka mu tchizi ndi m’zakudya zina. Choncho, anthu ameneŵa akadya zakudya za mtundu umenewo akhoza kudwala litsipa mwapafupipafupi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena