Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Anthu amene akukhulupirira kuti akudwala MCS ayenera kupita kwa dokotala wodziŵika bwino kuti apeze chithandizo choyenera. Kungakhale kupanda nzeru kusinthiratu zochita zanu zambiri, komwe mwinanso kungawonongetse ndalama zambiri, musanayezedwe mokwanira. Mwina atakupimani angapeze kuti muyenera kusintha zakudya kapena makhalidwe anu pang’ono chabe kuti muchepetse kapenanso kuthetseratu matendawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena