Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Malingaliro a anthu pankhani ya uchigaŵenga ndi osiyanasiyana kwambiri. Mwachitsanzo, m’mayiko ogaŵikana ndi nkhondo yapachiŵeniŵeni, ziwawa zochitidwa ndi gulu lina polimbana ndi gulu linzake anthu angazione ngati nkhondo yoyenera kapena monga uchigaŵenga, malinga ndi gulu lomwe lafunsidwalo. M’nkhani zino, mawu oti “uchigaŵenga” kwakukulukulu akunena za kuchita ziwawa n’cholinga choumiriza kuti pachitike chinachake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena