Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mboni za Yehova zimaona ntchito yawo yolalikira monga mmene mtumwi Paulo ankaionera, monga chinthu chofunikira kwa Akristu oona. Paulo anati: “Pakuti ngati ndilalikira Uthenga Wabwino ndilibe kanthu kakudzitamandira pakuti chondikakamiza ndigwidwa nacho [“pakuti ndimafunikira kutero,” NW].” (1 Akorinto 9:16) Komabe ntchito yawo yolalikira ndi yongodzipereka chifukwa anasankha okha kukhala ophunzira a Kristu, ndipo amakhala akudziŵa bwinobwino ntchito imene ayenera kuchita akapeza mwayi umenewu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena