Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Baibulo limati pali “Harmagedo,” imene imatchedwanso kuti “nkhondo ya tsiku lalikulu la Mulungu, Wamphamvuyonse.” Imeneyi si nkhondo ya anthu ayi, koma ndi nkhondo yochita kusankha imene Mulungu adzawonongere anthu ochita zoipa okha. Motero anthu sayenera kuganiza kuti chifukwa chakuti kuli Harmagedo ndiye kuti nkhondo zamasiku ano n’zabwinonso kapena kuti Mulungu amadalitsa nkhondozi.—Chivumbulutso 16:14, 16; 21:8.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena