Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Azibusa ena oganiza mopereŵera ankanena kuti malonda ogulitsa anthu mwankhanzaŵa Mulungu anali kugwirizana nawo. Motero, anthu ambiri amakhalabe ndi maganizo olakwika ameneŵa oti Baibulo limati palibe cholakwika ndi nkhanza zoterozo koma pamene ilo silitero. Chonde onani nkhani yakuti “Lingaliro la Baibulo: Kodi Mulungu Ankakondwera ndi Malonda a Ukapolo?” mu Galamukani! ya September 8, 2001.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena