Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Mkanda wa Baily umachitika chifukwa cha kuŵala kwa dzuŵa kukamadutsa m’zigwa za mwezi dzuŵalo lisanabisike lonse. Mawu akuti “mphete ya diamondi” amafotokoza mmene dzuŵa limaonekera likangotsala pang’ono kuti libisike lonse, pamene kachigawo kakang’ono ka dzuŵa kamakhala kakuwonekabe, zomwe zimaoneka ngati mphete yoyera yonyezimira, monga momwe mphete ya diamondi imaonekera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena