Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kwa nthaŵi yaitali ndithu, Akristu a Chiyuda a m’zaka 100 zoyambirira za Nyengo Yathu Ino omwe anali ku Yerusalemu ankasunga mbali zosiyanasiyana za Chilamulo cha Mose, mwina chifukwa chakuti: Chilamulocho chinali chochokera kwa Yehova. (Aroma 7:12, 14) Chinali chitawaloŵerera kwambiri anthu a Chiyuda n’kungosanduka mwambo wawo. (Machitidwe 21:20) Chinali lamulo lokhazikitsidwa ndi boma, ndipo aliyense wotsutsa chilamulocho akanangochititsa kuti uthenga wachikristu utsutsidwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena