Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mu nkhanizi, Galamukani! ikufotokoza maganizo akatswiri otchuka pa zakaleredwe ka ana, popeza kuti zimene amapeza pa nkhani zoterezi akachita kafukufuku zimatha kuthandiza makolo ndi kuwadziŵitsa zina ndi zina. Komabe, n’zoona kuti zimene ofufuzaŵa amapeza kaŵirikaŵiri amadzaziunikanso n’kusintha kunena zina. Koma si choncho ndi mfundo za m’Baibulo zimene Galamukani! imagwirizana nazo kwathunthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena