Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Baibulo la New World Translation of the Holy Scriptures, limene limafalitsidwa ndi Mboni za Yehova, ndi Baibulo limene linamasuliridwa mwamakono ndiponso mawu ake amagwirizana ndi mmene anthu amayankhulira panopo. Chinthu chofunika kwambiri m’Baibulo limeneli n’chakuti linabwezeretsa dzina la Mulungu pena paliponse pamene linayenera kukhalapo m’Malemba a Baibulo. Panopa, mabaibulo ameneŵa, athunthu kapena mbali yake yokha, oposa 122 miliyoni asindikizidwa m’zinenero zokwanira 45.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena