Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Chilamulo cha Mose chinali ndi malangizo okhudza katayidwe ka zonyansa, ukhondo, ndi kuika odwala kwaokha. Dr. H. O. Philips anafotokoza kuti “nkhani zokhudza kubereka, kutulukira matenda, kuchiza matenda, ndiponso khalidwe loteteza ku matenda zimene zili m’Baibulo n’zotsogola ndi zodalirika kwambiri kuposa zimene ankaphunzitsa Hippocrates.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena