Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu ophunzira kwambiri ndiponso asayansi otchuka amene anena poyera kuti amakhulupirira zoti pali “Wokonza Zinthu Wanzeru” ndi anthu monga Phillip E. Johnson amene amaphunzitsa za malamulo pa yunivesite ya ku California, Berkeley; katswiri wa zimene zimachitika m’kati mwa zinthu zamoyo Michael J. Behe, amene analemba buku lakuti Darwin’s Black Box—The Biochemical Challenge to Evolution; katswiri wa masamu William A. Dembski; katswiri wa kaganizidwe ka anthu Alvin Plantinga; akatswiri a sayansi ya kapangidwe ka zinthu John Polkinghorne ndi Freeman Dyson; katswiri wa sayansi ya zakuthambo Allan Sandage; ndi ena ambiri oti sitingakwanitse kuwatchula onse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena