Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Buku lotchedwa The Medical Journal of Australia limati “kuda nkhaŵa ndi maonekedwe ako ndi chizindikiro chofala cha matenda angapo a maganizo.” Matendaŵa ndi monga kuvutika maganizo, kulephera kudziletsa kuchita zinthu zinazake, ndi kuvutika kudya poopa kunenepa. Choncho matenda oda nkhaŵa kwambiri ndi maonekedwe a munthu angakhale ovuta kuwatulukira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena