Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Si kuti anthu onse amene amachita kuwapezera mwamuna kapena mkazi amakhala osasangalala. Mwachitsanzo, mu nthaŵi za m’Baibulo, Isake ndi Rebeka anachita kuwakonzera kuti akwatirane, ndipo Isake “anam’konda” Rebeka. (Genesis 24:67) Tingaphunzirepo chiyani pamenepa? Tingaphunzirepo kuti sibwino kunyoza miyambo ya kwanuko ngati sikusemphana ndi malamulo a Mulungu.—Machitidwe 5:29.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena