Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Nthawi zambiri, mowa wokwana magalamu seveni umachoka m’thupi pa ola lililonse. Kukula kwa botolo kapena tambula ya mowa kumasiyanasiyana malinga ndi dziko limene muli. A bungwe la World Health Organization amati m’mayiko ambiri, botolo limodzi kapena tambula imodzi ya mowa imakhala ndi mphamvu yoledzeretsa yokwana magalamu 10. Mlingo umenewu umapezeka mu mowa wamba wochuluka mamililita 250, vinyo wochuluka mamililita 100, kapena mowa wa m’gulu la kachasu wochuluka mamililita 30.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena