Mawu a M'munsi
b Pali anthu ochuluka zedi padziko lonse amene anachoka kwawo chifukwa cha mavuto a zandale kapena nkhondo. Kuti mudziwe mavuto awo, werengani nkhani zotsatizana zomwe zili mu Galamukani! ya February 8, 2002, ya mutu wakuti: “Kodi Othaŵa Nkhondo Adzapezadi Malo Okhazikika?”