Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Lemba la Levitiko 19:28 limati: “Musamadzicheka matupi anu chifukwa cha akufa.” Mwambo wachikunja umenewu, umene mwina cholinga chake chinali kusangalatsa milungu imene ankakhulupirira kuti imasamalira anthu akufa, ndi wosiyana ndi chizolowezi chodzivulaza chomwe tikuchifotokoza m’nkhani ino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena