Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu ena amanena kuti zaka zotchulidwa mu nkhani ya m’Baibulo imeneyi kwenikweni ndi miyezi. Komabe, nkhaniyo imati Aripakasadi anabereka Sela ali ndi zaka 35. Ngati zimenezi zikutanthauza miyezi 35, ndiye kuti Aripakasadi anakhala tate asanakwanitse zaka zitatu, zomwe mwachidziwikire n’zosatheka. Ndiponso, machaputala oyambirira a Genesis amasiyanitsa zaka, zomwe zimayendera dzuwa, ndi miyezi, yomwe imayendera mwezi.—Genesis 1:14-16; 7:11.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena