Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Anthu oweta agalu akhoza kusankha galu wamwamuna ndi wamkazi oti abereke ana n’cholinga choti anawo adzakhale ndi miyendo ifupiifupi kapena tsitsi lalitali kusiyana ndi makolo awo. Komabe, kusintha kumene kumabwera chifukwa chobereketsa agalu nthawi zambiri kumachitika chifukwa chakuti maselo ena a agaluwo sanagwire ntchito yake. Mwachitsanzo, pali agalu enaake amene amakhala aang’ono kwambiri chifukwa choti minofu yawo yokhala pakati pa mafupa sikula bwinobwino, ndipo mapeto ake agaluwa amakhala ngati abathwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena