Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Ngakhale kuti mawu akuti “mtundu” agwiritsidwa ntchito kwambiri mu nkhani ino, tiyenera kutchulapo kuti mawu amenewa si ofanana tanthauzo lake ndi mawu akuti “mtundu” amene ali m’buku la m’Baibulo la Genesis. M’Baibulo mawu akuti “mtundu” amatanthauza zinthu za m’gulu limodzi zomwe zikhoza kukhala zosiyanasiyana. Nthawi zambiri, zimene asayansi amati ndi kusintha kwa mtundu wa chamoyo n’kupanga chamoyo china, kwenikweni kumangokhala kusiyanasiyana kwa zamoyo za mtundu umodzi, monga momwe mawuwa akugwiritsidwira ntchito mu nkhani ya mu Genesis.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena