Mawu a M'munsi
g Dziwani izi: Genesis chaputala 1 chimati zomera ndi zinyama zizidzaberekana “monga mwa mitundu yawo.” (Genesis 1:12, 21, 24, 25) Komabe, mawu a m’Baibulo akuti “mtundu” si mawu asayansi ndipo sayenera kusokonezedwa ndi mawu akuti “mtundu” amene asayansi amagwiritsa ntchito.