Mawu a M'munsi
a Pofotokoza zomwe zinachitika pa tsiku loyamba la kulenga, mawu a Chihebri a kuwala amene anagwiritsidwa ntchito ndi akuti ʼohr, kutanthauza kuwala basi; koma ponena za tsiku lachinayi la kulenga, mawu amene anagwiritsidwa ntchito ndi akuti ma·ʼohrʹ, amene amatanthauza gwero la kuwalako.