Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Al-Khwārizmī anali katswiri wotchuka wa masamu ku Persia, m’zaka za m’ma 800, ndipo iyeyu ndiye anayambitsa masamu otchedwa ajebra, ndi njira za ku India zowerengetsera masamu, monga kulemba manambala ndi zilembo monga 1, 2, 3, . . . ndiponso anayambitsa nzeru zogwiritsa ntchito ziro powerengera masamu. Iyeyu ndiye anayambitsa mfundo zikuluzikulu zogwiritsidwa ntchito pamasamu. Mawu akuti “algorithm,” ogwiritsidwa ntchito pamasamu, anachokera padzina lake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena