Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nyama zambiri zimatha kusiyanitsa mitundu, ngakhale kuti zimaona mitunduyo mosiyana ndi mmene ife timaonera. Mwachitsanzo, agalu ali ndi magulu awiri okha a maselo ozindikira mitundu m’maso mwawo. Ali ndi gulu lozindikira mtundu wabluu ndiponso gulu lina lozindikira mtundu wa pakati pa kufiira ndi kubiriwira. Koma mbalame zina, zili ndi magulu anayi a maselo ozindikira mitundu ndipo zingathe kuzindikira mitundu ya kuwala imene anthu satha kuzindikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena