Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’pemphero la Ambuye, Yesu sananene kuti: “Choncho inu muzipemphera pemphero ili,” zimene zikanatsutsana ndi zomwe anali atangonena kumene. M’malo mwake iye anati: “Choncho inu muzipemphera motere.” (Mateyo 6:9-13) Kodi ankafuna kutiphunzitsa chiyani pamenepa? Malinga ndi zimene pemphero la Ambuye likusonyeza, tikamapemphera tiyenera kuganizira kwambiri zinthu zauzimu kuposa zofunika pamoyo wathu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena