Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Sikuti anthu onse angawasinthire mankhwala ngati mmene zinakhalira ndi Myra. Mwachitsanzo, anthu ena akadwala matenda opweteka kwambiri, amatha kupatsidwa mankhwala amphamvu omwe angathe kuwalowerera. Mankhwalawa amawamwa dokotala akuwayang’anira. Apa sitinganene kuti anthu oterewa akugwiritsa ntchito mankhwala molakwika.—Onani Miyambo 31:6.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena